< Masalimo 150 >

1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
Haleluja! Gloru Dion en Lia sanktejo, Gloru Lin en la firmaĵo de Lia forto.
2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
Gloru Lin por Liaj potencaj faroj, Gloru Lin laŭ Lia granda majesto.
3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
Gloru Lin per sonado de trumpeto, Gloru Lin per psaltero kaj harpo.
4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
Gloru Lin per tamburino kaj danco, Gloru Lin per kordinstrumentoj kaj fluto.
5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
Gloru Lin per laŭtaj cimbaloj, Gloru Lin per tintantaj cimbaloj.
6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.
Ĉio spiranta gloru la Eternulon. Haleluja!

< Masalimo 150 >