< Masalimo 150 >

1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
Halelujah. Chvalte Boha silného pro svatost jeho, chvalte jej pro rozšíření síly jeho.
2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
Chvalte jej ze všelijaké moci jeho, chvalte jej podlé veliké důstojnosti jeho.
3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
Chvalte jej zvukem trouby, chvalte jej na loutnu a citaru.
4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
Chvalte jej na buben a píšťalu, chvalte jej na husle a varhany.
5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
Chvalte jej na cymbály hlasité, chvalte jej na cymbály zvučné.
6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.
Všeliký duch chval Hospodina. Halelujah.

< Masalimo 150 >