< Masalimo 15 >

1 Salimo la Davide. Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika? Kodi ndani angathe kukhala mʼphiri lanu loyera?
Доамне, чине ва локуи ын кортул Тэу? Чине ва локуи пе мунтеле Тэу чел сфынт?
2 Munthu wa makhalidwe abwino, amene amachita zolungama, woyankhula choonadi chochokera mu mtima mwake,
Чел че умблэ ын неприхэнире, чел че фаче воя луй Думнезеу ши спуне адевэрул дин инимэ.
3 ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira, amene sachitira choyipa mnansi wake kapena kufalitsa mbiri yoyipa ya munthu mnzake,
Ачела ну клеветеште ку лимба луй, ну фаче рэу семенулуй сэу ши ну арункэ окарэ асупра апроапелуй сэу.
4 amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa. Koma amalemekeza amene amaopa Yehova, amene amakwaniritsa zomwe walonjeza ngakhale pamene zikumupweteka,
Ел привеште ку диспрец пе чел вредник де диспрецуит, дар чинстеште пе чей че се тем де Домнул. Ел ну-шь я ворба ынапой дакэ фаче ун журэмынт ын пагуба луй.
5 amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja ndipo salandira chiphuphu pofuna kutsutsa anthu osalakwa. Iye amene amachita zinthu zimenezi sadzagwedezeka konse.
Ел ну-шь дэ баний ку добындэ ши ну я митэ ымпотрива челуй невиноват. Чел че се поартэ аша, ну се клатинэ ничодатэ.

< Masalimo 15 >