< Masalimo 143 >
1 Salimo la Davide. Yehova imvani pemphero langa, mvetserani kulira kwanga kopempha chifundo; mwa kukhulupirika kwanu ndi chilungamo chanu bwerani kudzandithandiza.
Denggem ti kararagko, O Yahweh; dumngegka kadagiti panagpakpakaasik. Gapu iti kinapudnom ken kinalintegmo, sungbatannak!
2 Musazenge mlandu mtumiki wanu, pakuti palibe munthu wamoyo amene ndi wolungama pamaso panu.
Saanka a sumrek iti pangukoman a kaduam ti adipenmo, ta awan ti uray maysa a nalinteg iti imatangmo.
3 Mdani akundithamangitsa, iye wandipondereza pansi; wachititsa kuti ndikhale mu mdima ngati munthu amene anafa kale.
Kinamatdak dagiti kabusor; indumudomnak iti daga; pinagnaednak iti kasipngetan a kasla kadagiti nabayagen a natay.
4 Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga; mʼkati mwanga, mtima wanga uli ndi nkhawa.
Nabannog unayen ti espirituk iti kaunggak; awanen ti namnama ti pusok.
5 Ndimakumbukira masiku amakedzana; ndimalingalira za ntchito yanu yonse, ndimaganizira zimene manja anu anachita.
Nalagipko dagiti naglabas nga aldaw; ut-utobek dagiti amin nga ar-aramidmo, ut-utobek dagiti naaramidam.
6 Ndatambalitsa manja anga kwa Inu; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu monga nthaka yowuma. (Sela)
Inyunnatko dagiti imak nga agkararag kenka; mawaw ti kararuak kenka iti natikag a daga. (Selah)
7 Yehova ndiyankheni msanga; mzimu wanga ukufowoka. Musandibisire nkhope yanu, mwina ndidzakhala ngati iwo amene atsikira ku dzenje.
Sungbatannak kadi a dagus, O Yahweh, ta kumapkapuyen ti espirituk. Dinak ilemmengan, amangan no maituladak kadagiti mapan iti abut.
8 Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika, pakuti ine ndimadalira Inu. Mundisonyeze njira yoti ndiyendemo, pakuti kwa Inu nditukulira moyo wanga.
Ipangegmo kadi kaniak ti kinapudnom iti tulagmo iti agsapa, ta agtaltalekak kenka. Ipakitam kaniak ti dalan a rumbeng a pagnaak, ta intag-ayko ti kararuak kenka.
9 Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova, pakuti ndimabisala mwa Inu.
Ispalennak kadi, O Yahweh, kadagiti kabusorko; agkamangak kenka nga aglemmeng.
10 Phunzitseni kuchita chifuniro chanu, popeza ndinu Mulungu wanga; Mzimu wanu wabwino unditsogolere pa njira yanu yosalala.
Isuronak a mangaramid kadagiti pagayatam, ta sika ti Diosko. Idalannak koma ti naimbag nga Espiritum iti daga ti kinalinteg.
11 Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu tulutseni mʼmasautso anga.
Ipalubosmo nga agbiagak pay, O Yahweh, gapu iti naganmo; iti kinalintegmo, iruarmo ti kararuak iti pannakariribuk.
12 Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga; wonongani adani anga, pakuti ndine mtumiki wanu.
Iti kinapudnom iti tulagmo, putdem ken dadaelem dagiti amin a kabusor ti biagko, ta adipennak.