< Masalimo 141 >
1 Salimo la Davide. Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine. Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu.
Pieśń Dawida. PANIE, wołam do ciebie, pospiesz ku mnie; wysłuchaj mego głosu, gdy wołam do ciebie.
2 Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani; kukweza manja kwanga kukhale ngati nsembe yamadzulo.
Niech moja modlitwa będzie przed tobą [jak] kadzidło, [a] podniesienie moich rąk [jak] wieczorna ofiara.
3 Yehova ikani mlonda pakamwa panga; londerani khomo la pa milomo yanga.
PANIE, postaw straż przy moich ustach; strzeż drzwi moich warg.
4 Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa; kuchita ntchito zonyansa pamodzi ndi anthu amene amachita zoyipa; musalole kuti ndidye nawo zokoma zawo.
Nie skłaniaj mego serca ku złemu, abym nie popełniał czynów niegodziwych z ludźmi, którzy czynią nieprawość, i żebym się nie karmił ich rozkoszami.
5 Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo; andidzudzule ndiye mafuta pa mutu wanga. Mutu wanga sudzakana zimenezi. Komabe pemphero langa nthawi zonse ndi lotsutsana ndi ntchito za anthu ochita zoyipa.
Niech mnie bije sprawiedliwy, a [przyjmę to za] miłosierdzie; i niech mnie strofuje, a [będzie mi to] jak wyborny olejek, który nie zaszkodzi mojej głowie; bo jeszcze będę się modlił [w czasie] ich nieszczęścia.
6 Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri, ndipo anthu oyipa adzaphunzira kuti mawu anga anayankhulidwa bwino.
Gdy ich sędziowie będą zrzuceni do miejsc skalistych, usłyszą moje słowa, bo są wdzięczne.
7 Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
Jak [gdyby kto] rąbał i łupał [drwa] na ziemi, [tak] nasze kości są rozrzucone przy wejściu do grobu. (Sheol )
8 Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse; ndimathawira kwa Inu, musandipereke ku imfa.
Ale [podnoszę] swoje oczy do ciebie, BOŻE, Panie; tobie ufam, nie porzucaj mojej duszy.
9 Mundipulumutse ku misampha imene anditchera, ku makhwekhwe amene anthu oyipa andikonzera.
Strzeż mnie od sidła, [które] zastawili na mnie, i od pułapek czyniących nieprawość.
10 Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo, mpaka ine nditadutsa mwamtendere.
Niech niegodziwi wpadną w swoje sieci, podczas gdy ja ujdę cało.