< Masalimo 141 >
1 Salimo la Davide. Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine. Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu.
[Psalm lal David] Nga pang nu sum, LEUM GOD. Kasreyu inge! Lipsreyu ke nga pang nu sum.
2 Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani; kukweza manja kwanga kukhale ngati nsembe yamadzulo.
Eis pre luk in oana mwe kisa keng, Ac ke nga sralak pouk, eis in oana mwe kisa in eku.
3 Yehova ikani mlonda pakamwa panga; londerani khomo la pa milomo yanga.
LEUM GOD, filiya sie mwe karinginyen oalik, Ac mwe taran srungul lun ngoasrok.
4 Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa; kuchita ntchito zonyansa pamodzi ndi anthu amene amachita zoyipa; musalole kuti ndidye nawo zokoma zawo.
Ikolyuwi tuh nga in tia lungse oru ma koluk, Ac in tia wi mwet koluk ke ma elos oru. Lela nga in tiana ipeis ke kufwa lalos.
5 Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo; andidzudzule ndiye mafuta pa mutu wanga. Mutu wanga sudzakana zimenezi. Komabe pemphero langa nthawi zonse ndi lotsutsana ndi ntchito za anthu ochita zoyipa.
Sie mwet wo el ku in kaiyu ac aksuwosyeyu ke kulang lal, Tusruktu nga fah tia lela mwet koluk in akfulatyeyu, Mweyen nga pre in lain orekma koluk lalos pacl e nukewa.
6 Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri, ndipo anthu oyipa adzaphunzira kuti mawu anga anayankhulidwa bwino.
Ke mwet kol lalos sisyukla liki fulu in eot uh, Na mwet uh ac fah etu lah kas luk pwaye.
7 Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
Oana sak su lipikyuki nu ke ip srisrik, Ouinge sri kaclos ac fah oan oaclik sisken kulyuk uh. (Sheol )
8 Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse; ndimathawira kwa Inu, musandipereke ku imfa.
Tusruktu nga nuna lulalfongi kom, LEUM GOD Kulana. Nga suk molela lom; Nikmet lela nga in misa!
9 Mundipulumutse ku misampha imene anditchera, ku makhwekhwe amene anthu oyipa andikonzera.
Moliyula liki mwe kwasrip su elos orala in sruokyu, Ac liki sruhf lun mwet orekma koluk.
10 Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo, mpaka ine nditadutsa mwamtendere.
Lela tuh mwet koluk in putatyang nu in sruhf lalos sifacna A nga fahla na siska, ac tia sruoh.