< Masalimo 140 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Landitseni Yehova kwa anthu oyipa; tetezeni kwa anthu ankhanza,
Ispalennak, O Yahweh, kadagiti nadangkes; salaknibannak kadagiti naranggas a tattao.
2 amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa ndi kuyambitsa nkhondo tsiku lililonse.
Mangpangpanggepda iti dakes kadagiti pusoda; inaldaw a mangirugrugida iti riri.
3 Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka; pa milomo yawo pali ululu wa mamba. (Sela)
Makasugat dagiti dilada a kas kadagiti uleg; adda kadagiti bibigda ti gita ti karasaen. (Selah)
4 Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa; tchinjirizeni kwa anthu ankhanza amene amakonza zokola mapazi anga.
Salaknibannak, O Yahweh, kadagiti ima dagiti nadangkes; saluadannak kadagiti naranggas a tattao a mangpangpanggep a mangdangran kaniak.
5 Anthu odzikuza anditchera msampha mobisika; iwo atchera zingwe za maukonde awo ndipo anditchera misampha pa njira yanga. (Sela)
Nangiwayat dagiti natangsit a tattao iti pakaipalab-ogak; nangiwarasda iti iket; nangiwayatda iti pakasiloak. (Selah)
6 Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.” Imvani kupempha kwanga Yehova.
Kinunak kenni Yahweh, “Sika ti Diosko; dumngegka kadagiti panagdawdawatko iti asi.”
7 Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu, mumateteza mutu wanga tsiku lankhondo.
O Yahweh nga Apok, napigsaka a mangispal; salsalaknibam ti ulok iti aldaw ti gubat.
8 Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova; musalole kuti zokonza zawo zitheke, mwina iwo adzayamba kunyada. (Sela)
O Yahweh, saanmo a patgan dagiti tarigagay dagiti nadangkes; saanmo nga itulok nga agballigi dagiti panggepda. (Selah)
9 Mitu ya amene andizungulira iphimbidwe ndi masautso amene milomo yawo yayambitsa.
Natangsit dagiti nakapalawlaw kaniak; bay-am a ti kinadakes dagiti bibigda ti mangdadael kadakuada.
10 Makala amoto agwere pa iwo; aponyedwe pa moto, mʼmaenje amatope, asatulukemonso.
Bay-am a matnag dagiti beggang kadakuada; ipurwakmo ida iti apuy, kadagiti mangliwengliweng nga abut, a saanda pulos a makaruk-at.
11 Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko; choyipa chilondole anthu ankhanza.
Saan koma a mapatalged ditoy lubong ti siasinoman a mangibagbaga kadagiti dakes a banbanag kadagiti sabali; anupen koma iti kinadakes ti naranggas a tao tapno dadaelenna isuna.
12 Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka, ndipo amateteza zolinga za anthu osowa.
Ammok nga ikaluya ni Yahweh dagiti mairurrurumen, ken ikalinteganna dagiti agkasapulan.
13 Zoonadi anthu olungama adzatamanda dzina lanu, ndipo anthu owongoka mtima adzakhala pamaso panu.
Awan duadua a pagyamanan dagiti nalinteg a tattao ti naganmo; agnaed dagiti nalinteg a tattao iti presensiam.