< Masalimo 138 >
1 Salimo la Davide. Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zokutamandani pamaso pa “milungu.”
I KAPINA komui jan nan monion i, i pan kakaule kin komui mon dikedik en ani kan.
2 Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera ndipo ndidzayamika dzina lanu chifukwa cha chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu, pakuti Inu mwakuza dzina lanu ndi mawu anu kupambana zinthu zonse.
I pan kakaudok inen won japwilim omui im en kaudok jaraui, o kapina mar omui, pweki omui kalanan o melel, pwe kom kotin kalinanada mar omui jan meakaroj ki omui majan.
3 Pamene ndinayitana, munandiyankha; munandisandutsa wamphamvu ndi wolimba mtima.
Ni ai likwir won komui, komui ap kotin mani ia, o kom kamanada monion i melel.
4 Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova, pamene amva mawu a pakamwa panu.
Main leowa, nanmarki en jappa karoj pan kapina komui, ni ar pan ron majan en jilan ir.
5 Iwo ayimbe za njira za Yehova, pakuti ulemerero wa Yehova ndi waukulu.
O re pan kauleki al en leowa kan, pwe linan en leowa meid laud.
6 Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa, koma anthu onyada amawadziwira chapatali.
Pwe leowa me lapalap ap kotin ireron me tikitik kan, o a kotin mani me aklapalap, jan ni waja doo.
7 Ngakhale ndiyende pakati pa masautso, mumasunga moyo wanga; mumatambasula dzanja lanu kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga, mumandipulumutsa ndi dzanja lanu lamanja.
Ni ai weweid nan kamajak melel, kom kin kotin kolekol on ia maur i, o kom kin kapa won lim omui pan makar en ai imwintiti kan, o kom jaunja ia da ki lim omui maun.
8 Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine; chikondi chanu chosasinthika Yehova, ndi chosatha musasiye ntchito ya manja anu.
leowa pan kotin wiawia ia. Main leowa, omui kalanan me pan potopot eta; Kom der kotin muei jan dodok en lim omui kan.