< Masalimo 138 >

1 Salimo la Davide. Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zokutamandani pamaso pa “milungu.”
E MILILANI aku au ia oe me kuu naau a pau, Imua o na'kua e hoolea aku ai au ia oe.
2 Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera ndipo ndidzayamika dzina lanu chifukwa cha chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu, pakuti Inu mwakuza dzina lanu ndi mawu anu kupambana zinthu zonse.
E kulou hoomana au ma kou luakini hoano, A e mililani aku i kou inoa, No kou lokomaikai a me ka oiaio; No ka mea, ua hookaulana oe i kau olelo mamua o kou inoa a pau.
3 Pamene ndinayitana, munandiyankha; munandisandutsa wamphamvu ndi wolimba mtima.
I ka la a'u i kahea aku ai ia oe, Alaila, hoolohe mai no oe ia'u, Ua hooikaika mai oe ia'u, me ka ikaika ma kuu uhane.
4 Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova, pamene amva mawu a pakamwa panu.
E mililani aku na'lii a pau o ka honua ia oe, e Iehova, Ia lakou e lohe ai i na huaolelo a kou waha.
5 Iwo ayimbe za njira za Yehova, pakuti ulemerero wa Yehova ndi waukulu.
E oli no lakou i na aoao o Iehova, No ka mea, nui no ka nani o Iehova.
6 Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa, koma anthu onyada amawadziwira chapatali.
Ua kiekie loa o Iehova, ua nana mai nei i ka poe haahaa; Aka, ua ike no oia i ka poe hookiekie ma kahi loihi.
7 Ngakhale ndiyende pakati pa masautso, mumasunga moyo wanga; mumatambasula dzanja lanu kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga, mumandipulumutsa ndi dzanja lanu lamanja.
Ina paha e hele wau iloko o ka pilikia, Nau no wau e hoola mai. Maluna o ka huhu o kou poe enemi, e o mai ai oe i kou lima, A me kou lima akau oe e hoopakele mai ai ia'u.
8 Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine; chikondi chanu chosasinthika Yehova, ndi chosatha musasiye ntchito ya manja anu.
E hoopaa no o Iehova i na mea e pili mai ai ia'u; Ua mau loa no kou lokomaikai, e Iehova, Mai haalele oe i na hana a kou mau lima.

< Masalimo 138 >