< Masalimo 136 >

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
Praise the Lord, for he is good: for his mercy endureth for ever.
2 Yamikani Mulungu wa milungu.
Praise ye the God of gods: for his mercy endureth for ever.
3 Yamikani Ambuye wa ambuye,
Praise ye the Lord of lords: for his mercy endureth for ever.
4 Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
Who alone doth great wonders: for his mercy endureth for ever.
5 Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
Who made the heavens in understanding: for his mercy endureth for ever.
6 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
Who established the earth above the waters: for his mercy endureth for ever.
7 Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
Who made the great lights: for his mercy endureth for ever.
8 Dzuwa lilamulire usana,
The sun to rule over the day: for his mercy endureth for ever.
9 Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
The moon and the stars to rule the night: for his mercy endureth for ever.
10 Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
Who smote Egypt with their firstborn: for his mercy endureth for ever.
11 Natulutsa Israeli pakati pawo,
Who brought Israel from among them: for his mercy endureth for ever.
12 Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
With a mighty hand and a stretched out arm: for his mercy endureth for ever.
13 Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
Who divided the Red Sea into parts: for his mercy endureth for ever.
14 Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
And brought out Israel through the midst thereof: for his mercy endureth for ever.
15 Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
And overthrew Pharao and his host in the Red Sea: for his mercy endureth for ever.
16 Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
Who led his people through the desert: for his mercy endureth for ever.
17 Amene anakantha mafumu akuluakulu,
Who smote great kings: for his mercy endureth for ever.
18 Napha mafumu amphamvu,
And slew strong kings: for his mercy endureth for ever.
19 Siloni mfumu ya Aamori,
Sehon king of the Amorrhites: for his mercy endureth for ever.
20 Ogi mfumu ya Basani,
And Og king of Basan: for his mercy endureth for ever.
21 Napereka dziko lawo ngati cholowa,
And he gave their land for an inheritance: for his mercy endureth for ever.
22 Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
For an inheritance to his servant Israel: for his mercy endureth for ever.
23 Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
For he was mindful of us in our affliction: for his mercy endureth for ever.
24 Amene anatimasula kwa adani athu,
And he redeemed us from our enemies: for his mercy endureth for ever.
25 Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
Who giveth food to all flesh: for his mercy endureth for ever.
26 Yamikani Mulungu wakumwamba,
Give glory to the God of heaven: for his mercy endureth for ever.

< Masalimo 136 >