< Masalimo 136 >
1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
Give ye thanks unto Jehovah, for he is good; for his loving-kindness [endureth] for ever:
2 Yamikani Mulungu wa milungu.
Give thanks unto the God of gods, for his loving-kindness [endureth] for ever;
3 Yamikani Ambuye wa ambuye,
Give thanks unto the Lord of lords, for his loving-kindness [endureth] for ever.
4 Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
To him who alone doeth great wonders, for his loving-kindness [endureth] for ever:
5 Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
To him that by understanding made the heavens, for his loving-kindness [endureth] for ever;
6 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
To him that stretched out the earth above the waters, for his loving-kindness [endureth] for ever;
7 Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
To him that made great lights, for his loving-kindness [endureth] for ever;
8 Dzuwa lilamulire usana,
The sun for rule over the day, for his loving-kindness [endureth] for ever,
9 Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
The moon and stars for rule over the night, for his loving-kindness [endureth] for ever:
10 Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
To him that smote Egypt in their firstborn, for his loving-kindness [endureth] for ever,
11 Natulutsa Israeli pakati pawo,
And brought out Israel from among them, for his loving-kindness [endureth] for ever,
12 Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
With a powerful hand and with a stretched-out arm, for his loving-kindness [endureth] for ever;
13 Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
To him that divided the Red sea into parts, for his loving-kindness [endureth] for ever,
14 Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
And made Israel to pass through the midst of it, for his loving-kindness [endureth] for ever,
15 Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
And overturned Pharaoh and his host in the Red sea, for his loving-kindness [endureth] for ever;
16 Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
To him that led his people through the wilderness, for his loving-kindness [endureth] for ever;
17 Amene anakantha mafumu akuluakulu,
To him that smote great kings, for his loving-kindness [endureth] for ever,
18 Napha mafumu amphamvu,
And slew famous kings, for his loving-kindness [endureth] for ever;
19 Siloni mfumu ya Aamori,
Sihon king of the Amorites, for his loving-kindness [endureth] for ever,
And Og king of Bashan, for his loving-kindness [endureth] for ever;
21 Napereka dziko lawo ngati cholowa,
And gave their land for an inheritance, for his loving-kindness [endureth] for ever,
22 Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
An inheritance unto Israel his servant, for his loving-kindness [endureth] for ever:
23 Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
Who hath remembered us in our low estate, for his loving-kindness [endureth] for ever;
24 Amene anatimasula kwa adani athu,
And hath delivered us from our oppressors, for his loving-kindness [endureth] for ever:
25 Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
Who giveth food to all flesh, for his loving-kindness [endureth] for ever.
26 Yamikani Mulungu wakumwamba,
Give ye thanks unto the God of the heavens; for his loving-kindness [endureth] for ever.