< Masalimo 133 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
En visa Davids i högre choren. Si, huru godt och lustigt är det, att bröder bo endrägteliga tillsammans;
2 Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
Såsom kosteligit balsam är, det af Aarons hufvud flyter neder i allt hans skägg, det nederflyter uppå hans kläder;
3 Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.
Såsom Hermons dagg, och den på Zions berg nederfaller; ty dersammastäds lofvar Herren välsignelse och lif till evig tid.

< Masalimo 133 >