< Masalimo 133 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
Ятэ че плэкут ши че дулче есте сэ локуяскэ фраций ымпреунэ!
2 Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
Есте ка унтделемнул де прец, каре, турнат пе капул луй, се кобоарэ пе барбэ, пе барба луй Аарон, се кобоарэ пе марӂиня вешминтелор луй.
3 Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.
Есте ка роуа Хермонулуй, каре се кобоарэ пе мунций Сионулуй, кэч аколо дэ Домнул бинекувынтаря, вяца, пентру вешничие.

< Masalimo 133 >