< Masalimo 133 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
Sabo-Pionjonañe, a i Davide Akore ty hasoa naho ty hafanjàka’ ty fitraofañ’ ìna’ o mpirahalahio!
2 Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
Manahake ty solike sarotse añambone’e eo, miroroñe an-tsomotse, an-tanteahe’ i Aharone mb’eo, mitsiritsiok’ añ’ olon-tsaro’e mireparepay.
3 Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.
Hambañe ami’ty mika’ i Kermone mivotrak’ amo vohi’ i Tsiôneo; amy nañoriza’ Iehovà fitahiañey, eka! haveloñe nainai’e.

< Masalimo 133 >