< Masalimo 133 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
Se, hvor godt og hvor lifligt er det, at Brødre ogsaa bo tilsammen,
2 Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
som den gode Olie paa Hovedet, hvilken nedflyder paa Skægget, Arons Skæg, der gaar ned over Sømmen af hans Klædebon;
3 Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.
som Hermons Dug, der falder ned over Zions Bjerge; thi der har Herren beskikket Velsignelsen, Livet indtil evig Tid.

< Masalimo 133 >