< Masalimo 131 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
Господе! Не надима се срце моје, нити се узносе очи моје; нити идем на велико, ни на оно што је више од мене.
2 Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
Смеран сам и кротак душом својом, као дете крај матере; као дете душа је моја у мени.
3 Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Нек се узда Израиљ у Господа одсад и довека.

< Masalimo 131 >