< Masalimo 13 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
Керівнику хору. Псалом Давидів. Доки, Господи? Невже Ти забув мене навіки? Доки ховатимеш обличчя Своє від мене?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
Доки тяжкі роздуми носитиму я в душі своїй [і] муку в серці своєму день у день? Доки величатиметься ворог мій наді мною?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
Зглянься ж, дай мені відповідь, Господи, Боже мій! Очі мої просвіти, щоб сном смертним я не заснув,
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
щоб не говорив мій ворог: «Я здолав його!» Щоб не раділи супротивники мої, коли я похитнуся.
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
Я ж бо на милість Твою покладаю надію, радітиме серце моє через порятунок, [посланий] Тобою,
6 Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.
співатиму я Господеві, бо Він виявив до мене прихильність.

< Masalimo 13 >