< Masalimo 13 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
Az éneklőmesternek; Dávid zsoltára.
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
Uram, meddig felejtkezel el rólam végképen? Meddig rejted el orczádat tőlem?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
Meddig tanakodjam lelkemben, bánkódjam szívemben naponként? Meddig hatalmaskodik az én ellenségem rajtam?
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
Nézz ide, felelj nékem, Uram Istenem; világosítsd meg szemeimet, hogy el ne aludjam a halálra;
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
Hogy ne mondja ellenségem: meggyőztem őt; háborgatóim ne örüljenek, hogy tántorgok.
6 Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.
Mert én a te kegyelmedben bíztam, örüljön a szívem a te segítségednek; hadd énekeljek az Úrnak, hogy jót tett velem!