< Masalimo 127 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
Süleyman'ın hac ilahisi Evi RAB yapmazsa, Yapıcılar boşuna didinir. Kenti RAB korumazsa, Bekçi boşuna bekler.
2 Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
Boşuna erken kalkıp Geç yatıyorsunuz. Ey zahmetle kazanılan ekmeği yiyenler, RAB sevdiklerinin rahat uyumasını sağlar.
3 Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
Çocuklar RAB'bin verdiği bir armağandır, Rahmin ürünü bir ödüldür.
4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
Yiğidin elinde nasılsa oklar, Öyledir gençlikte doğan çocuklar.
5 Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.
Ne mutlu ok kılıfı onlarla dolu insana! Kent kapısında hasımlarıyla tartışırken Utanç duymayacaklar.

< Masalimo 127 >