< Masalimo 127 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
En visa Salomos, i högre choren. Om Herren icke bygger huset, så arbeta de fåfängt, som derpå bygga; om Herren icke förvarar staden, så vaka väktarena fåfängt.
2 Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
Det är fåfängt, att I bittida uppstån, och sent gån till hvilo, och äten edart bröd med sorg; ty han gifver det sina vänner, vid de sofva.
3 Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
Si, barn äro en Herrans gåfva, och lifsfrukt är en skänk.
4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
Lika som skott uti en stark mans hand, så äro ock de unge dränger.
5 Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.
Säll är den som sitt koger af dem full hafver; de komma icke på skam, då de med sina fiendar handla i portenom.

< Masalimo 127 >