< Masalimo 127 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
Pieśń stopni dla Salomona. Jeźli Pan domu nie zbuduje, próżno pracują ci, którzy go budują; jeźli Pan nie będzie strzegł miasta, próżno czuje ten, który go strzeże.
2 Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
Próżno macie rano wstawać, długo siadać, i jeść chleb boleści, ponieważ Pan umiłowanemu swemu sen daje.
3 Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
Oto dziatki są dziedzictwem od Pana, a płód żywota nagrodą.
4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
Jako strzały w ręku mocarza, tak są dziatki, które się darzą.
5 Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.
Błogosławiony mąż, który niemi napełnił sajdak swój; nie będą zawstydzani, gdy się w bramie rozpierać będą z nieprzyjaciołmi swymi.

< Masalimo 127 >