< Masalimo 126 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
Oluyimba nga balinnya amadaala. Mukama bwe yakomyawo abawaŋŋanguse ba Sayuuni, twafaanana ng’abaloota.
2 Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
Olwo akamwa kaffe ne kajjula enseko, ne nnimi zaffe ne ziyimba ennyimba ez’essanyu. Amawanga ne gagamba nti, “Mukama abakoledde ebikulu.”
3 Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
Mukama atukoledde ebikulu, kyetuvudde tusanyuka.
4 Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
Otuzze obuggya, Ayi Mukama, tufaanane ng’emigga egikulukutira mu lusenyi.
5 Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
Abo abasiga nga bakaaba amaziga, baliyimba ennyimba ez’essanyu nga bakungula.
6 Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.
Oyo agenda ng’akaaba ng’atwala ensigo okusiga; alikomawo ng’ayimba ennyimba ez’essanyu ng’aleeta ebinywa bye.

< Masalimo 126 >