< Masalimo 126 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
都もうでの歌 主がシオンの繁栄を回復されたとき、われらは夢みる者のようであった。
2 Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
その時われらの口は笑いで満たされ、われらの舌は喜びの声で満たされた。その時「主は彼らのために大いなる事をなされた」と言った者が、もろもろの国民の中にあった。
3 Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
主はわれらのために大いなる事をなされたので、われらは喜んだ。
4 Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
主よ、どうか、われらの繁栄を、ネゲブの川のように回復してください。
5 Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
涙をもって種まく者は、喜びの声をもって刈り取る。
6 Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.
種を携え、涙を流して出て行く者は、束を携え、喜びの声をあげて帰ってくるであろう。

< Masalimo 126 >