< Masalimo 125 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
Tangtlaeng Laa BOEIPA dongah aka pangtung rhoek tah Zion tlang bangla, kumhal ah tuen pawt tih ngol.
2 Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Jerusalem kaepvai kah tlang rhoek tah amah ham coeng ni. Te dongah BOEIPA tah a pilnam a kaepvai ah, tahae lamkah neh kumhal duela om.
3 Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
Halangnah mancai loh aka dueng rhoek kah hmulung te naan boel saeh. Te daengah ni aka dueng loh a kut te dumlai la a hlah pawt eh.
4 Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
BOEIPA aw aka then taeng neh, a lungbuei ah aka thuem taengah tah hlampan pah.
5 Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.
Tedae BOEIPA aw, amih a kael la aka mael rhoek neh boethae aka saii te a tueih ni. Israel soah rhoepnah om saeh.

< Masalimo 125 >