< Masalimo 125 >
1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
Hina Godema dafawaneyale dawa: su dunu da mae fogole amola mae iguguli, Saione Goumi agoane diala.
2 Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Goumi da Yelusaleme moilai bai bagade amo sisiga: i defele, Hina Gode da Ea fi gaga: musa: , eso huluane mae fisili, sisiga: le ouligilala.
3 Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
Wadela: i hamosu dunu da eso huluane moloidafa dunu ilia soge hame ouligi laluma. Ilia da amo hamoi ganiaba, moloidafa dunu da wadela: i hou hamona: nobela: ?
4 Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
Hina Gode! Moloidafa dunu amo da Dia hamoma: ne sia: su nabawane hamosa, ilima hou ida: iwane hamoma.
5 Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.
Be Di da wadela: i hamosu dunuma se dabe iasea, gilisili dunu amo da Dia moloi logo fisiagasea, ilima se dabe ima. Isala: ili fi ilima olofosu dialumu da defea!