< Masalimo 123 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu amene mumakhala kumwamba.
Пісня проча́н.
2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo, monga momwenso maso a mdzakazi amayangʼana mʼdzanja la dona wake, choncho maso athu ali kwa Yehova Mulungu wathu, mpaka atichitire chifundo.
Ото бо, як очі рабів до руки́ їх панів, як очі неві́льниці — до руки́ її пані, отак наші очі до Го́спода, нашого Бога, аж поки не зми́лується Він над нами!
3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo, pakuti tapirira chitonzo chachikulu.
Помилуй нас, Господи, помилуй нас, бо пого́рди ми до́сить наси́тились!
4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza, chitonzo chachikulu kuchokera kwa anthu onyada.
Душа наша наси́тилась до́сить собі: від безпе́чних — нару́ги, від пи́шних — пого́рди!

< Masalimo 123 >