< Masalimo 123 >
1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu amene mumakhala kumwamba.
I KIN sarada wong komui, me kotikot nanlang.
2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo, monga momwenso maso a mdzakazi amayangʼana mʼdzanja la dona wake, choncho maso athu ali kwa Yehova Mulungu wathu, mpaka atichitire chifundo.
Kilang, duen mas en ladu kan kin kilekilang lim en ar saumas akan, o duen mas en lidu kan kin kilekilang a saumas li, iduen mas at kin ariri Ieowa at Kot, a lao kotin maki ong kit.
3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo, pakuti tapirira chitonzo chachikulu.
Maing Ieowa, kom kotin maki ong, kotin maki ong kit! Pwe kit me dir en namenok.
4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza, chitonzo chachikulu kuchokera kwa anthu onyada.
Moniong i toutouki en me sued akan ar mamale kin kit o en me aklapalap akan ar kanamenok kin kit.