< Masalimo 123 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu amene mumakhala kumwamba.
Kathutkung: Panuekhoeh, tami tangawn ni Hezekiah a ti awh Kalvan kho a tungkhung kaawm e nang koe doeh ka ngaihawi.
2 Taonani, monga momwe maso a akapolo amayangʼana mʼdzanja la mbuye wawo, monga momwenso maso a mdzakazi amayangʼana mʼdzanja la dona wake, choncho maso athu ali kwa Yehova Mulungu wathu, mpaka atichitire chifundo.
Sanpanaw ni a bawipa kut a ngaihawi e patetlah thoseh, Sannunaw ni a bawipa kut a ngaihawi e patetlah thoseh, kaimouh ni lungmanae ka coe awh hoehroukrak BAWIPA Cathut doeh na ngaihawi awh.
3 Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo, pakuti tapirira chitonzo chachikulu.
Oe BAWIPA, kaimouh na lungma haw. Kaimouh na lungma haw. Bangkongtetpawiteh, banglah noutnahoehnae teh koung ka boum awh toe.
4 Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza, chitonzo chachikulu kuchokera kwa anthu onyada.
Kaimae hringnae teh, ka kâoupnaw ni yeiraipo saknae hai thoseh, lunglenpansa lah kaawm naw ni banglah noutnahoehnae hai thoseh, koung ka boum awh toe.

< Masalimo 123 >