< Masalimo 122 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
Ɔsoroforo dwom. Dawid de. Me ne wɔn a wosee me sɛ, “Ma yɛnkɔ Awurade fi” no ani gyei.
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
Yegyinagyina wʼaponkɛse ano, Yerusalem.
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
Wɔakyekyere Yerusalem yiye sɛ kuropɔn wahyehyɛ mu nneɛma fɛfɛ.
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
Ɛhɔ na mmusuakuw no kɔ, Awurade mmusuakuw no, Wɔkɔkamfo Awurade din, sɛnea nhyehyɛe a wɔde ama Israel no te.
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
Ɛhɔ na atemmu nhengua no sisi, Dawid fi nhengua no.
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
Monsrɛ asomdwoe mma Yerusalem se, “Ma wɔn a wɔdɔ wo no nnya bammɔ.
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
Ma asomdwoe mmra wʼafasu mu na bammɔ mmra wʼaban mu.”
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
Me nuanom ne me nnamfonom nti, mɛka se, “Asomdwoe ntena wo mu.”
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.
Awurade yɛn Nyankopɔn fi nti, mɛhwehwɛ wo yiyeyɛ.

< Masalimo 122 >