< Masalimo 122 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
Nilifurahi waliponiambia, “Na twende kwenye Nyumba ya Yahwe.”
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
Ee Yerusalemu, miguu yetu imesimama ndani ya malango yako!
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
Ee Yerusalemu, uliojengwa kama mji uliopangiliwa kwa umakini!
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
Makabila huenda juu Yerusalemu, makabila ya Yahwe; kama ushuhuda wa Israeli, kulishukuru jina la Yahwe.
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
Huko viliwekwa viti vya hukumu, viti vya enzi vya nyumba ya Daudi.
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
Ombeni kwa ajili ya amani ya Yerusalemu! “Wote wakupendao wawe na amani.
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
Amani iwepo ndani ya kuta zako ili ikutetee, na wawe na amani ndani ya ngome zako.”
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
Kwa ajili ya ndugu zangu na rafiki zangu nitasema, “Amani iwe ndani yenu.”
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.
Kwa ajili ya Yahwe Mungu wetu, nitatafuta mema kwa ajili yako.

< Masalimo 122 >