< Masalimo 122 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
Een lied Hammaaloth, van David. Ik verblijd mij in degenen, die tot mij zeggen: Wij zullen in het huis des HEEREN gaan.
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
Onze voeten zijn staande in uw poorten, o Jeruzalem!
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
Jeruzalem is gebouwd, als een stad, die wel samengevoegd is;
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
Waarheen de stammen opgaan, de stammen des HEEREN, tot de getuigenis Israels, om den Naam des HEEREN te danken.
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
Want daar zijn de stoelen des gerichts gezet, de stoelen van het huis van David.
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
Bidt om den vrede van Jeruzalem; wel moeten zij varen, die u beminnen.
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
Vrede zij in uw vesting, welvaren in uw paleizen.
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
Om mijner broederen en mijner vrienden wil, zal ik nu spreken, vrede zij in u!
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.
Om des huizes des HEEREN, onzes Gods wil, zal ik het goede voor u zoeken.

< Masalimo 122 >