< Masalimo 122 >

1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
Давидова песен на възкачванията. Зарадвах се, когато ми рекоха: Да отидем в дома Господен.
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
Ето, нозете ни стоят Отвътре портите ти Ерусалиме.
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
Ерусалиме, който си съграден, Като град сглобен в едно;
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
Гдето възлизат племената, Господните племена. Според надеждите на Израиля, За да славят името Господно.
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
Защото там са поставени престоли за съд, Престолите на Давидовия дом.
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
Молитствувайте за мира на Ерусалим; Нека благоденствуват ония, които те обичат!
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
Мир да бъде отвътре стените ти, Благоденствие в палатите ти!
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
Заради братята и другарите си Ще кажа сега: Мир да е в тебе!
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.
Заради дома на Господа нашия Бог Ще търся доброто ти.

< Masalimo 122 >