< Masalimo 121 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
«Yuⱪiriƣa qiⱪix nahxisi» Kɵzlirimni taƣlar tǝrǝpkǝ kɵtürüp ⱪaraymǝn; Mening yardimim ⱪǝyǝrdin kelur?
2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Mening yardimim Pǝrwǝrdigardindur; Asman-zeminni Yaratⱪuqidindur.
3 Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
U putungni ⱨeq teyildurmaydu; Seni saⱪliƣuqi ⱨeq mügdimǝydu!
4 Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
Mana, ⱪara, Israilni saⱪliƣuqi ⱨǝm mügdimǝydu, ⱨǝm uhlimaydu!
5 Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
Pǝrwǝrdigar sening saⱪliƣuqingdur; Pǝrwǝrdigar ong yeningdiki sayiwǝndur.
6 Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
Ⱪuyax kündüzdǝ, ay keqidǝ sanga zǝrǝr yǝtküzmǝydu;
7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
Pǝrwǝrdigar barliⱪ yamanliⱪtin seni saⱪlaydu; U jeningni saⱪlaydu;
8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Pǝrwǝrdigar qiⱪixingni, kirixingni, Buningdin keyin ǝbǝdil’ǝbǝdgiqǝ saⱪlaydu.

< Masalimo 121 >