< Masalimo 121 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
Itataas ko ang aking mga mata sa mga bundok. Mula saan manggagaling ang aking saklolo?
2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Ang saklolo sa akin ay nanggagaling kay Yahweh, na gumawa ng langit at lupa.
3 Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
Hindi niya papayagang madulas ang paa mo; siya na nag-iingat sa iyo ay hindi iidlip.
4 Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
Tingnan mo, ang tagapangalaga ng Israel ay hindi kailanman iidlip o matutulog.
5 Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
Tagapangalaga ninyo si Yahweh; si Yahweh ay lilim sa inyong kanang kamay.
6 Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
Hindi ka masasaktan ng araw sa umaga, ni ng buwan sa gabi.
7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
Iingatan ka ni Yahweh sa lahat ng kapahamakan, at iingatan niya ang iyong buhay.
8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Iingatan ni Yahweh ang lahat ng iyong ginagawa ngayon at magpakailanman.

< Masalimo 121 >