< Masalimo 121 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
Keima kadah'in thinglhanglam kavei, hichea kon a khu eipanpi hung hintem?
2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Vanle lei sem pa Paka a kon a eipanpi hung ahi.
3 Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
Aman nangma nakipalsah louding; nachingpa chu ihmu louding ahi.
4 Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
Tahbeh'in Israel chingpa chu itihchan hijongleh ihmu lhulou ding ahilouleh ihmu louding ahi.
5 Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
Yahweh Pakai amatah chu nachingpa ahi! Ama nakom a ading jingin nahoidohna lim in apang jinge.
6 Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
Sun leh nisan nasangpeh pontin, janleh lhavah injong nasubeipon te.
7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
Yahweh Pakai in thilse jousea nahoidohsah in tin nahinkho chingjing nante.
8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Yahweh Pakai in tuapat tonsot gei in navai kondoh leh nahung vailhun in nachingjing tahen.

< Masalimo 121 >