< Masalimo 120 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
En mi angustia, mi llanto subió al Señor, y él me dio una respuesta.
2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
Oh Señor, sé el salvador de mi alma de los labios mentirosos y de la lengua del engaño.
3 Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
¿Qué castigo te dará? ¿Qué más te hará él, lengua falsa?
4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
Flechas afiladas del fuerte y fuego ardiente.
5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
La aflicción es mía porque soy extraño en Mesec, y vivo en las tiendas de Cedar.
6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
Mi alma ha estado viviendo por mucho tiempo con los que odian la paz.
7 Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
Estoy a favor de la paz; pero cuando digo eso, están a favor de la guerra.

< Masalimo 120 >