< Masalimo 120 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
Canticum graduum. Ad Dominum cum tribularer clamavi: et exaudivit me.
2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
Domine libera animam meam a labiis iniquis, et a lingua dolosa.
3 Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
Quid detur tibi, aut quid apponatur tibi ad linguam dolosam?
4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
Sagittae potentis acutae, cum carbonibus desolatoriis.
5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
Heu mihi, quia incolatus meus prolongatus est: habitavi cum habitantibus Cedar:
6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
multum incola fuit anima mea.
7 Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
Cum his, qui oderunt pacem, eram pacificus: cum loquebar illis, impugnabant me gratis.

< Masalimo 120 >