Preface
Bibles
+
CHW
HMO
X
<
h8267
>
X
<
^
>
<
>
<
Masalimo
120
>
1
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
שיר המעלות אל יהוה בצרתה לי קראתי ויענני׃
2
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
יהוה הצילה נפשי משפת שקר מלשון רמיה׃
3
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
מה יתן לך ומה יסיף לך לשון רמיה׃
4
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
חצי גבור שנונים עם גחלי רתמים׃
5
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
אויה לי כי גרתי משך שכנתי עם אהלי קדר׃
6
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
רבת שכנה לה נפשי עם שונא שלום׃
7
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
אני שלום וכי אדבר המה למלחמה׃
<
Masalimo
120
>
Go to
>
Bookmark
/
Concordance
/
Maps
/
Report Issue
The world's first Holy Bible un-translation!