Preface
Bibles
+
CHW
CUT
X
<
h7200G
>
X
<
^
>
<
>
<
Masalimo
120
>
1
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
上行(或譯登階,下同)之詩。 我在急難中求告耶和華, 他就應允我。
2
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
耶和華啊,求你救我脫離說謊的嘴唇和詭詐的舌頭!
3
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
詭詐的舌頭啊,要給你甚麼呢? 要拿甚麼加給你呢?
4
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
就是勇士的利箭和羅騰木 的炭火。
5
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
我寄居在米設, 住在基達帳棚之中,有禍了!
6
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
我與那恨惡和睦的人許久同住。
7
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
我願和睦, 但我發言,他們就要爭戰。
<
Masalimo
120
>
Go to
>
Bookmark
/
Concordance
/
Maps
/
Report Issue
The world's first Holy Bible un-translation!