< Masalimo 120 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
Tangtlaeng Laa Kamah kah citcai khuiah BOEIPA te ka khue tih kai n'doo.
2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
BOEIPA aw ka hinglu he laithae hmuilai lamkah neh palyal ol lamloh huul lah.
3 Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
Palyal ol te nang taengah bahamnim m'paek vetih bahamnim nang taengah hang koei eh?
4 Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
Hlangrhalh kah thaltang khaw hlingcet alh bangla sum yipkip.
5 Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
Meshek ah ka bakuep tih Kedar dap ah kho ka sak dongah kai ngawn tah ka tuisawih coeng!
6 Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
Rhoepnah aka hmuhuet taengah ka hinglu loh kho puet a sak coeng.
7 Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.
Kai loh rhoepnah ka thui vaengah amih te caemtloek la thoouh.

< Masalimo 120 >