< Masalimo 12 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide. Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika; okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
Kumqondisi wokuhlabela. Ngendlela yesheminithi. Ihubo likaDavida. Siza Thixo, ngoba kabasekho abakholwayo; abathembekileyo sebenyamalele kabasekho ebantwini.
2 Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
Bonke baqamba amanga kubomakhelwane babo; izindebe zabo eziyengayo zihlezi zikhuluma inkohliso esezinhliziyweni zabo.
3 Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo ndi pakamwa paliponse podzikuza.
Sengathi uThixo angaziquma zonke izindebe ezikhohlisayo kanye laluphi ulimi oluzikhukhumezayo
4 Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu; pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
oluthi, “Sizanqoba ngendimi zethu; izindebe zethu zizasilwela ngubani oyinkosi yethu na?”
5 “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu ndi kubuwula kwa anthu osowa, Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova, “Ndidzawateteza kwa owazunza.”
“Ngenxa yokuncindezelwa kwabayanga lokububula kwabaswelayo, sengizavuka khathesi,” kutsho uThixo. “Ngizabavikela kulabo ababachukuluzayo.”
6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri.
Njalo amazwi kaThixo amsulwa, njengesiliva esicengwe esithandweni somlilo esebumba, njengegolide elihlanjululwe kasikhombisa.
7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
Oh Thixo, uzahlala usiphephisile njalo usivikele ebantwini ababi nini lanini.
8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.
Ababi bayaklamasa santando nxa bebona izinto ezilihlazo zidunyiswa ngabantu.

< Masalimo 12 >