< Masalimo 12 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide. Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika; okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
Veisuunjohtajalle; matalassa äänialassa; Daavidin virsi. Auta, Herra, sillä hurskaat ovat hävinneet, uskolliset ovat kadonneet ihmislasten joukosta.
2 Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
He puhuvat valhetta toinen toisellensa, puhuvat liukkain huulin, kaksimielisin sydämin.
3 Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo ndi pakamwa paliponse podzikuza.
Hävittäköön Herra kaikki liukkaat huulet, kielen, joka kerskuen puhuu,
4 Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu; pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
ne, jotka sanovat: "Kielemme voimalla me olemme väkevät; huulemme ovat meidän tukemme; kuka on meille herra?"
5 “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu ndi kubuwula kwa anthu osowa, Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova, “Ndidzawateteza kwa owazunza.”
"Kurjien sorron tähden, köyhien huokausten tähden minä nyt nousen", sanoo Herra, "tuon pelastuksen sille, joka sitä huoaten ikävöitsee".
6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri.
Herran sanat ovat selkeitä sanoja, hopeata, joka kirkkaana valuu sulattimesta maahan, seitsenkertaisesti puhdistettua.
7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
Sinä, Herra, varjelet heitä, suojelet hänet iäti tältä sukukunnalta.
8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.
Yltympäri jumalattomat rehentelevät, kun kataluus pääsee valtaan ihmislasten seassa.

< Masalimo 12 >