< Masalimo 118 >

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino; pakuti chikondi chake chosasinthika ndi chosatha.
DANKE leowa, pwe i me man, pwe a kalanan pan potopot eta.
2 Israeli anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”
Ijrael en indinda: A kalanan pan potopot eta.
3 Banja la Aaroni linene kuti, “Chikondi chake ndi chosatha.”
Kadaudok en Aron en indinda: A kalanan pan potopot eta.
4 Iwo amene amaopa Yehova anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”
Me majak Kot akan en inda: A kalanan pan potopot eta.
5 Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova, ndipo Iye anayankha pondichotsa mʼmasautsowo.
Ni ai apwal akan i likwir won leowa; leowa kotin mani ia er o kotin kajone ia dier waja jaledok.
6 Yehova ali nane; sindidzachita mantha. Munthu angandichite chiyani?
leowa kin kotin ieian ia, i jota majak, da me aramaj akan kak wiai on ia?
7 Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa. Ndidzayangʼana adani anga mwachipambano.
Ieowa kin kotin ieian ia nan pun en me jauaja ia, o i pan peren kida, me kailon kin ia.
8 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira munthu.
Me mau, en liki Ieowa, jan kaporoporeki aramaj akan.
9 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira mafumu.
Me mau en liki Ieowa, jan kaporoporeki jaupeidi kan.
10 Anthu a mitundu yonse anandizinga, koma mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Men liki kan karoj kapil ia penaer; a ni mar en Ieowa i kaloe ir edier.
11 Anandizinga mbali zonse, koma mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Re kapil ia penaer waja karoj, a ni mar en Ieowa i pan kaloe irail edier.
12 Anandizinga ngati njuchi, koma anatha msanga ngati moto wapaminga; mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Re kapil ia penaer dueta lonlap akan, a re kunlar dueta kinjiniai nan tuka; ni mar en Ieowa i kaloe irail edier.
13 Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa, koma Yehova anandithandiza.
Re woki ia, pwe i ne pupedi, a Ieowa kotin jauaja iaer.
14 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.
Ieowa iei ai kel o ai kaul, o i me kotin wiala ai jaunkamaur.
15 Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano ukumveka mʼmatenti a anthu olungama mtima kuti: “Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!
Kaul en kaperen o kamaur kin wiaui nan im en me pun kan, lim en Ieowa pali maun kin kapwaiada dodok manaman.
16 Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!”
Pali maun en Ieowa me ileile, pali maun en Ieowa kin kapwaiada dodok manaman.
17 Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo ndipo ndidzalalika za ntchito ya Yehova.
I jota pan mela, pwe memaur eta o padaki duen wiawian Ieowa.
18 Yehova wandilanga koopsa, koma sanandipereke ku imfa.
Ieowa kotin kaloke ia laud, ap jota meuid on, i en mela.
19 Tsekulireni zipata zachilungamo, kuti ndifike kudzayamika Yehova.
Komail ritinadan ia wanim en pun, pwe i waja me i pan pedelon ia, pwen danke Ieowa.
20 Ichi ndicho chipata cha Yehova chimene olungama mtima okha adzalowerapo.
Iet wanim en Ieowa, waja me pun kan pan pedelon ia.
21 Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha; mwakhala chipulumutso changa.
I danke komui, pwe kom kotin erekier ai kapakap o jauaja ia.
22 Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana wasanduka wapangodya;
Takai o me pwin jauje kajelar, wialar takain pukakaim.
23 Yehova ndiye wachita zimenezi ndipo nʼzodabwitsa pamaso pathu.
Mepukat wiauier ian ron Ieowa, meid kapuriamui ni maj at!
24 Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga; tiyeni tikondwere ndi kusangalala nalo.
let ran o, me Ieowa kotin wiadar, kitail en popol o peren kida i.
25 Inu Yehova, tipulumutseni; Yehova, tipambanitseni.
O Main Ieowa, kom kotin jauaja! O Main Ieowa, kom kotin kapwaiada!
26 Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova. Tikukudalitsani kuchokera ku nyumba ya Yehova.
Meid kapinan me kotido ni mar en Ieowa! Kit kapai komail da, me kijan toun tanpaj en Ieowa.
27 Yehova ndi Mulungu, ndipo kuwala kwake kwatiwunikira Ife. Lowani nawo pa mʼdipiti wa ku chikondwerero mutanyamula nthambi mʼdzanja lanu, mpaka ku nyanga za guwa.
Ieowa iei Kot, o i me kotin kamarain kitail er; jaliedi men mairon ni oj en pei jaraui!
28 Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani; Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakukwezani.
Komui ai Kot, o i pan danke komui; ai Kot, i pan kalinanada komui.
29 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino; pakuti chikondi chake chosasinthika ndi chosatha.
Danke Ieowa, pwe i me mau, pwe a kalanan pan potopot eta.

< Masalimo 118 >