< Masalimo 118 >

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino; pakuti chikondi chake chosasinthika ndi chosatha.
Agyamantayo kenni Yahweh, ta naimbag isuna, ta agtalinaed iti agnanayon ti kinapudnona iti tulagna.
2 Israeli anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”
Ibaga koma ti Israel, “Agtalinaed iti agnanayon ti kinapudnona iti tulagna.”
3 Banja la Aaroni linene kuti, “Chikondi chake ndi chosatha.”
Ibaga koma ti balay ni Aaron, “Agtalinaed iti agnanayon ti kinapudnona iti tulagna.”
4 Iwo amene amaopa Yehova anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”
Ibaga koma dagiti agbuteng kenni Yahweh, “Agtalinaed iti agnanayon ti kinapudnona iti tulagna.”
5 Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova, ndipo Iye anayankha pondichotsa mʼmasautsowo.
Immawagak kenni Yahweh idi marigrigatanak; sinungbatannak ni Yahweh ken winayawayaannak.
6 Yehova ali nane; sindidzachita mantha. Munthu angandichite chiyani?
Adda kaniak ni Yahweh; saanakto nga agbuteng; ania ti maaramidan ti tao kaniak?
7 Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa. Ndidzayangʼana adani anga mwachipambano.
Adda ni Yahweh iti sibayko a mangtulong kaniak; kumitaak nga addaan iti panagballigi kadagiti manggurgura kaniak.
8 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira munthu.
Nasaysayaat ti agkamang kenni Yahweh ngem ti agtalek iti tao.
9 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira mafumu.
Nasaysayaat ti agkamang kenni Yahweh ngem ti agtalek kadagiti prinsipe.
10 Anthu a mitundu yonse anandizinga, koma mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Pinalawlawandak dagiti amin a nasion; babaen iti nagan ni Yahweh ket pinarmekko ida.
11 Anandizinga mbali zonse, koma mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Pinalawlawandak; wen, pinalawlawandak; babaen iti nagan ni Yahweh ket pinarmekko ida.
12 Anandizinga ngati njuchi, koma anatha msanga ngati moto wapaminga; mʼdzina la Yehova ndinawawononga.
Pinalawlawandak a kasla alimbubuyog; napukawda a dagus a kasla ti apuy kadagiti sisiit; iti nagan ni Yahweh pinarmekko ida.
13 Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa, koma Yehova anandithandiza.
Dinarupdak tapno matumbaak, ngem tinulongannak ni Yahweh.
14 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.
Ni Yahweh ti pigsa ken rag-ok ken isuna ti mangisalsalakan kaniak
15 Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano ukumveka mʼmatenti a anthu olungama mtima kuti: “Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!
Mangngeg ti narag-o a pukkaw ti panagballigi kadagiti tolda dagiti nalinteg; mangparparmek ti kannawan nga ima ni Yahweh.
16 Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!”
Naitan-ok ti kannawan nga ima ni Yahweh; mangparparmek ti kannawan nga ima ni Yahweh.
17 Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo ndipo ndidzalalika za ntchito ya Yehova.
Saanakto a matay, ngem ketdi agbiagak tapno iwaragawagko dagiti aramid ni Yahweh.
18 Yehova wandilanga koopsa, koma sanandipereke ku imfa.
Dinusanak iti nakaro ni Yahweh; ngem saannak nga impaima iti patay.
19 Tsekulireni zipata zachilungamo, kuti ndifike kudzayamika Yehova.
Ilukatyo man kaniak dagiti ruangan ti kinalinteg; sumrekak kadagitoy ket agyamanak kenni Yahweh.
20 Ichi ndicho chipata cha Yehova chimene olungama mtima okha adzalowerapo.
Daytoy ti ruangan ni Yahweh; pagserkan daytoy dagiti nalinteg.
21 Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha; mwakhala chipulumutso changa.
Agyamanak kenka, ta sinungbatannak ken sika ti nangisalakan kaniak.
22 Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana wasanduka wapangodya;
Ti bato nga imbelleng dagiti agipatpatakder ket nagbalin a kangrunaan a pasuli a bato.
23 Yehova ndiye wachita zimenezi ndipo nʼzodabwitsa pamaso pathu.
Aramid daytoy ni Yahweh; nakakaskasdaaw daytoy iti imatangtayo.
24 Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga; tiyeni tikondwere ndi kusangalala nalo.
Daytoy ti aldaw a nagtignay ni Yahweh; agragsak ken agrambaktayo iti daytoy.
25 Inu Yehova, tipulumutseni; Yehova, tipambanitseni.
Pangngaasim, O Yahweh, pagballigiennakami! Pangngaasim, O Yahweh, ikkannakami iti kinadur-as!
26 Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova. Tikukudalitsani kuchokera ku nyumba ya Yehova.
Nagasat ti tao nga umay babaen iti nagan ni Yahweh, bendisionandakayo manipud iti balay ni Yahweh.
27 Yehova ndi Mulungu, ndipo kuwala kwake kwatiwunikira Ife. Lowani nawo pa mʼdipiti wa ku chikondwerero mutanyamula nthambi mʼdzanja lanu, mpaka ku nyanga za guwa.
Dios ni Yahweh, ken inikkannatayo iti lawag; igalutyo dagiti daton kadagiti sara ti altar.
28 Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani; Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakukwezani.
Sika ti Diosko, ken agyamanak kenka; sika ti Diosko; itan-okka.
29 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino; pakuti chikondi chake chosasinthika ndi chosatha.
O, agyamantayo kenni Yahweh; ta naimbag isuna; ta agtalinaed iti agnanayon ti kinapudnona iti tulagna.

< Masalimo 118 >