< Masalimo 117 >

1 Tamandani Yehova, inu anthu a mitundu yonse; mulemekezeni Iye, inu mitundu ya anthu.
Whakamoemititia a Ihowa, e nga tauiwi katoa: whakamoemititia ia, e nga iwi katoa.
2 Pakuti chikondi chake pa ife ndi chachikulu, ndipo kukhulupirika kwa Yehova nʼkosatha. Tamandani Yehova.
He nui hoki tana mahi tohu ki a tatou: e mau ana hoki te pono o Ihowa ake ake. Whakamoemititia a Ihowa.

< Masalimo 117 >