< Masalimo 116 >

1 Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo.
Юбеск пе Домнул, кэч Ел ауде гласул меу, черериле меле.
2 Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga.
Да, Ел Шь-а плекат урекя спре мине, де ачея-Л вой кема тоатэ вяца мя.
3 Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
Мэ ынфэшурасерэ легэтуриле морций ши м-апукасерэ судориле мормынтулуй; ерам прадэ неказулуй ши дурерий. (Sheol h7585)
4 Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!”
Дар ам кемат Нумеле Домнулуй ши ам зис: „Доамне, мынтуеште-мь суфлетул!”
5 Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
Домнул есте милостив ши дрепт ши Думнезеул ностру есте плин де ындураре.
6 Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa.
Домнул пэзеште пе чей фэрэ рэутате: ерам ненорочит де тот, дар Ел м-а мынтуит.
7 Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma.
Ынтоарче-те, суфлете, ла одихна та, кэч Домнул ць-а фэкут бине!
8 Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe,
Да, Ту мь-ай избэвит суфлетул де ла моарте, окий дин лакримь ши пичоареле де кэдере.
9 kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
Вой умбла ынаинтя Домнулуй, пе пэмынтул челор вий.
10 Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati, “Ndasautsidwa kwambiri.”
Авям дрептате кынд зичям: „Сунт фоарте ненорочит!”
11 Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.”
Ын нелиништя мя, зичям: „Орьче ом есте ыншелэтор.”
12 Ndingamubwezere chiyani Yehova, chifukwa cha zokoma zake zonse zimene wandichitira?
Кум вой рэсплэти Домнулуй тоате бинефачериле Луй фацэ де мине?
13 Ndidzakweza chikho cha chipulumutso ndipo ndidzayitana dzina la Yehova.
Вой ынэлца пахарул избэвирилор ши вой кема Нумеле Домнулуй;
14 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse.
ымь вой ымплини журуинцеле фэкуте Домнулуй, ын фаца ынтрегулуй Сэу попор.
15 Imfa ya anthu oyera mtima ndi yamtengowapatali pamaso pa Yehova.
Скумпэ есте ынаинтя Домнулуй моартя челор юбиць де Ел.
16 Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu: ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; Inu mwamasula maunyolo anga.
Аскултэ-мэ, Доамне, кэч сунт робул Тэу: робул Тэу, фиул роабей Тале, ши Ту мь-ай десфэкут легэтуриле!
17 Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu ndipo ndidzayitanira pa dzina la Yehova.
Ыць вой адуче о жертфэ де мулцумире ши вой кема Нумеле Домнулуй;
18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,
ымь вой ымплини журуинцеле фэкуте Домнулуй ын фаца ынтрегулуй Сэу попор,
19 mʼmabwalo a nyumba ya Yehova, mʼkati mwako iwe Yerusalemu. Tamandani Yehova.
ын курциле Касей Домнулуй, ын мижлокул тэу, Иерусалиме! Лэудаць пе Домнул!

< Masalimo 116 >