< Masalimo 116 >

1 Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo.
Ég elska Drottin, því að hann heyrir bænir mínar – og svarar þeim.
2 Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga.
Meðan ég dreg andann mun ég biðja til hans, því að hann lítur niður og hlustar á mig.
3 Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
Ég horfðist í augu við dauðann – var hræddur og hnípinn. (Sheol h7585)
4 Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!”
Þá hvíslaði ég: „Drottinn, frelsaðu mig!“
5 Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
Náðugur er Drottinn og góður er hann!
6 Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa.
Drottinn hlífir vondaufum og styrkir hjálparvana.
7 Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma.
Nú get ég slakað á og verið rór, því að Drottinn hefur gert mikla hluti fyrir mig.
8 Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe,
Hann hefur bjargað mér frá dauða, augum mínum frá gráti og fótum mínum frá hrösun.
9 kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
Ég fæ að lifa! Já, lifa með honum hér á jörðu!
10 Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati, “Ndasautsidwa kwambiri.”
Þegar ég átti erfitt hugsaði ég:
11 Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.”
Þeir segja ósatt, að allt muni snúast mér í hag.
12 Ndingamubwezere chiyani Yehova, chifukwa cha zokoma zake zonse zimene wandichitira?
En nú, hvernig get ég nú endurgoldið Drottni góðverk hans við mig?
13 Ndidzakweza chikho cha chipulumutso ndipo ndidzayitana dzina la Yehova.
Ég vil lyfta bikarnum og vínberjalegi að fórn, þakka honum lífið.
14 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse.
Fórnina sem ég lofaði Drottni, færi ég nú í allra augsýn.
15 Imfa ya anthu oyera mtima ndi yamtengowapatali pamaso pa Yehova.
Hann elskar vini sína og lætur þá ekki deyja án gildrar ástæðu.
16 Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu: ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; Inu mwamasula maunyolo anga.
Drottinn, þú hefur leyst fjötra mína, því vil ég þjóna þér af öllu hjarta.
17 Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu ndipo ndidzayitanira pa dzina la Yehova.
Ég vil lofa þig og færa þér þakkarfórn.
18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,
Í forgörðum musteris Drottins í Jerúsalem vil ég –
19 mʼmabwalo a nyumba ya Yehova, mʼkati mwako iwe Yerusalemu. Tamandani Yehova.
og það í augsýn allra – færa honum allt sem ég hafði lofað. Dýrð sé Drottni!

< Masalimo 116 >