< Masalimo 116 >
1 Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo.
to love: lover for to hear: hear LORD [obj] voice my supplication my
2 Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga.
for to stretch ear his to/for me and in/on/with day my to call: call to
3 Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
to surround me cord death and terror hell: Sheol to find me distress and sorrow to find (Sheol )
4 Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!”
and in/on/with name LORD to call: call to Please! LORD to escape [emph?] soul my
5 Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
gracious LORD and righteous and God our to have compassion
6 Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa.
to keep: guard simple LORD to languish and to/for me to save
7 Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma.
to return: return soul my to/for resting your for LORD to wean upon you
8 Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe,
for to rescue soul my from death [obj] eye my from tears [obj] foot my from falling
9 kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
to go: walk to/for face: before LORD in/on/with land: country/planet [the] alive
10 Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati, “Ndasautsidwa kwambiri.”
be faithful for to speak: speak I to afflict much
11 Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.”
I to say in/on/with to hurry I all [the] man to lie
12 Ndingamubwezere chiyani Yehova, chifukwa cha zokoma zake zonse zimene wandichitira?
what? to return: pay to/for LORD all benefit his upon me
13 Ndidzakweza chikho cha chipulumutso ndipo ndidzayitana dzina la Yehova.
cup salvation to lift: raise and in/on/with name LORD to call: call to
14 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse.
vow my to/for LORD to complete before [to] please to/for all people his
15 Imfa ya anthu oyera mtima ndi yamtengowapatali pamaso pa Yehova.
precious in/on/with eye: seeing LORD [the] death [to] to/for pious his
16 Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu: ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; Inu mwamasula maunyolo anga.
Please! LORD for I servant/slave your I servant/slave your son: child maidservant your to open to/for bond my
17 Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu ndipo ndidzayitanira pa dzina la Yehova.
to/for you to sacrifice sacrifice thanksgiving and in/on/with name LORD to call: call to
18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,
vow my to/for LORD to complete before [to] please to/for all people his
19 mʼmabwalo a nyumba ya Yehova, mʼkati mwako iwe Yerusalemu. Tamandani Yehova.
in/on/with court house: temple LORD in/on/with midst your Jerusalem to boast: praise LORD