< Masalimo 115 >

1 Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi koma ulemerero ukhale pa dzina lanu, chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika ndiponso chifukwa cha kukhulupirika kwanu.
Ɛnyɛ yɛn, Awurade, ɛnyɛ yɛn, na wo din na anuonyam nka, wʼadɔe ne wo nokwaredi nti.
2 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti, “Mulungu wawo ali kuti?”
Adɛn nti na aman no bisa se, “Wɔn Nyankopɔn wɔ he?”
3 Mulungu wathu ali kumwamba; Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa.
Yɛn Nyankopɔn wɔ ɔsoro; nea ɔpɛ biara na ɔyɛ.
4 Koma mafano awo ndi siliva ndi golide, opangidwa ndi manja a anthu.
Nanso wɔn ahoni yɛ dwetɛ ne sikakɔkɔɔ a wɔde onipa nsa na ayɛ.
5 Pakamwa ali napo koma sayankhula, maso ali nawo koma sapenya;
Wɔwɔ ano, nanso wontumi nkasa; wɔwɔ ani, nanso wonhu ade.
6 makutu ali nawo koma samva, mphuno ali nazo koma sanunkhiza;
Wɔwɔ aso, nanso wɔnte asɛm; wɔwɔ hwene, nanso wɔnte hua.
7 manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu; mapazi ali nawo koma sayenda; kapena pakhosi pawo kutulutsa mawu.
Wɔwɔ nsa, nanso wɔnte nka; wɔwɔ anan, nanso wɔnnantew. Wontumi mma nnyigyei bi mfi wɔn mene mu.
8 Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo, chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo.
Wɔn a wɔyɛɛ ahoni no bɛyɛ sɛ wɔn ara, saa ara na wɔn a wɔde wɔn ho to wɔn so no bɛyɛ.
9 Inu Aisraeli, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
Mo Israelfo nyinaa, momfa mo ho nto Awurade so, ɔyɛ mo boafo ne kyɛm.
10 Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova; Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.
Ao Aaronfi, momfa mo ho nto Awurade so, ɔyɛ mo boafo ne kyɛm.
11 Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
Mo a musuro no, momfa mo ho nto Awurade so, ɔyɛ mo boafo ne kyɛm.
12 Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israeli, adzadalitsa nyumba ya Aaroni,
Awurade kae yɛn na obehyira yɛn: Obehyira Israelfi, obehyira Aaronfi
13 adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova; aangʼono ndi aakulu omwe.
Obehyira wɔn a wosuro Awurade, nketewa ne akɛse nyinaa.
14 Yehova akuwonjezereni madalitso; inuyo pamodzi ndi ana anu.
Awurade mma wʼase nnɔ, wo ne wo mma.
15 Mudalitsidwe ndi Yehova, Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Awurade nhyira wo, ɔsoro ne asase Yɛfo no.
16 Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.
Ɔsorosoro tɔnn yɛ Awurade de, nanso asase de, ɔde ama onipa.
17 Si anthu akufa amene amatamanda Yehova, amene amatsikira kuli chete;
Ɛnyɛ awufo na wɔkamfo Awurade wɔn a wɔkɔ fam dinn no.
18 ndi ife amene timatamanda Yehova, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Yehova.
Yɛn na yɛma Awurade so nnɛ ne daa nyinaa. Monkamfo Awurade.

< Masalimo 115 >