< Masalimo 115 >
1 Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi koma ulemerero ukhale pa dzina lanu, chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika ndiponso chifukwa cha kukhulupirika kwanu.
Ba gare mu ba, ya Ubangiji, ba gare mu ba amma ga sunanka yă sami ɗaukaka, saboda ƙaunarka da amincinka.
2 Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti, “Mulungu wawo ali kuti?”
Me ya sa al’ummai suke cewa, “Ina Allahnsu?”
3 Mulungu wathu ali kumwamba; Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa.
Allahnmu yana a sama; yana yin duk abin da ya ga dama.
4 Koma mafano awo ndi siliva ndi golide, opangidwa ndi manja a anthu.
Amma gumakansu azurfa da zinariya ne, da hannuwan mutane suka yi.
5 Pakamwa ali napo koma sayankhula, maso ali nawo koma sapenya;
Suna da bakuna, amma ba sa magana, idanu, amma ba sa gani;
6 makutu ali nawo koma samva, mphuno ali nazo koma sanunkhiza;
suna da kunnuwa, amma ba sa ji, hanci, amma ba sa jin ƙanshi
7 manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu; mapazi ali nawo koma sayenda; kapena pakhosi pawo kutulutsa mawu.
suna da hannuwa, amma ba sa iya taɓa kome, ƙafafu, amma ba sa iya tafiya; ba sa iya ce wani abu da maƙogwaronsu.
8 Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo, chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo.
Masu yinsu za su zama kamar su, haka kuma zai kasance da duk wanda ya dogara da su.
9 Inu Aisraeli, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
Ya gidan Isra’ila, ku dogara ga Ubangiji, shi ne mai taimakonsu da garkuwarsu.
10 Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova; Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.
Ya gidan Haruna, ku dogara ga Ubangiji, shi ne mai taimakonsu da garkuwarsu.
11 Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
Ku da kuke tsoronsa, ku dogara ga Ubangiji, shi ne mai taimakonsu da garkuwarsu.
12 Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israeli, adzadalitsa nyumba ya Aaroni,
Ubangiji yakan tuna da mu zai kuma albarkace mu. Zai albarkace gidan Isra’ila, zai albarkace gidan Haruna,
13 adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova; aangʼono ndi aakulu omwe.
zai albarkace waɗanda suke tsoron Ubangiji, manya da ƙanana duka.
14 Yehova akuwonjezereni madalitso; inuyo pamodzi ndi ana anu.
Bari Ubangiji yă sa ku ƙaru, da ku da’ya’yanku.
15 Mudalitsidwe ndi Yehova, Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Bari Ubangiji yă albarkace ku, shi Mahalicci sama da ƙasa.
16 Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.
Saman sammai na Ubangiji ne, amma ya ba da duniya ga mutum.
17 Si anthu akufa amene amatamanda Yehova, amene amatsikira kuli chete;
Ba matattu ba ne masu yabon Ubangiji, waɗanda suke gangara zuwa wurin da ake shiru;
18 ndi ife amene timatamanda Yehova, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Yehova.
mu ne masu ɗaukaka Ubangiji, yanzu da har abada kuma. Yabi Ubangiji.